Chifukwa “Chimene Ndinabwerera M’dziko” (Mateyu 21:23-46; 22:15-46)

KOPERANI

Mwina Mungakondenso Kudziwa Izi

YESU—NDI NJIRA, CHOONADI NDI MOYO

Yesu Analepheretsa Afarisi Kuti Amugwire

Yesu anasowetsa chonena Afarisi, Asaduki komanso gulu la anthu omwe ankamutsutsa.

YESU—NDI NJIRA, CHOONADI NDI MOYO

Anadzudzula Atsogoleri Achipembedzo Omwe Ankamutsutsa

N’chifukwa chiyani sanalekere zinthu zolakwika zimene atsogoleri achipembedzo ankachita?

YESU—NDI NJIRA, CHOONADI NDI MOYO

Mafanizo Awiri Onena za Munda wa Mpesa

Werengani nkhaniyi kuti mudziwe zimene fanizo la munthu amene anapempha ana ake kuti akagwire ntchito m’munda wake komanso zimene fanizo la munthu amene anasiyira antchito oipa munda wake wampesa limatanthauza.

MAVIDIYO

“Mulungu Anamuika Kukhala Ambuye Ndi Khristu” (Mbali Yoyamba)

N’chiyani chimakupangitsani kukhulupirira kuti Mulungu anamuika Yesu kukhala Ambuye ndi Khristu?

MAVIDIYO

“Mulungu Anamuika Kukhala Ambuye Ndi Khristu” (Mbali Yachiwiri)

Onerani vidiyoyi kuti muzikhulupirira kwambiri Yesu.