Pitani ku nkhani yake

Colombia

 

2018-05-28

COLOMBIA

A Mboni Anapatsidwa Mphoto ndi Bungwe Loona Ntchito Yomasulira M’chinenero cha Manja ku Colombia

A Mboni za Yehova ku Colombia analandira mphoto ziwiri powayamikira chifukwa cha ntchito yawo yomasulira m’Chinenero Chamanja cha ku Colombia.