Lambirani Yehova Mudakali Achinyamata
Yehova amafuna kuti tizikhala anthu oyamikira. Tiyeni tione njira imodzi imene tingasonyezere kuti ndife oyamikira.
Mwina Mungakondenso Kudziwa Izi
KHALANI BWENZI LA YEHOVA
Lambirani Yehova Mudakali Achinyamata (Nyimbo 133)
Kumbukirani Mlengi wanu Wamkulu mudakali achinyamata.
ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA
Zoti Ana Achite
Gwiritsani ntchito zinthu zosangalatsa zimenezi, nkhani zochokera m’Baibulo komanso makadi a anthu otchulidwa m’Baibulo pophunzitsa ana mfundo za m’Baibulo.