GALAMUKANI! January 2015 | Kodi Moyo Unayamba Bwanji?

Kodi yankho la funsoli lingatengere ngati mumakhulupirira kuti kuli Mulungu kapena ayi?

NKHANI YAPACHIKUTO

Kodi Moyo Unayamba Bwanji?

N’chifukwa chiyani asayansi ena zimawavuta kukhulupirira kuti zamoyo zinasintha kuchokera ku zinthu zina?

NKHANI YAPACHIKUTO

Mafunso Awiri Omwe Tiyenera Kudziwa Mayankho Ake

Werengani nkhaniyi kuti mudziwe ngati muyenera kukhulupirira zimene anthu omwe amati zamoyo zinasintha kuchokera ku zinthu zina amanena.

NKHANI YAPACHIKUTO

Baibulo Lili Ndi Mayankho Ogwira Mtima

Kodi n’chiyani chinathandiza wasayansi yemwe ankalimbikitsa anthu kuti asamakhulupirire Mulungu, kuti ayambe kukhulupirira Mulungu?

KODI ZINANGOCHITIKA ZOKHA?

Chisa cha Njuchi

Kodi njuchi zakhala zikudziwa zinthu zotani zokhudza kugwiritsa ntchito malo mosamala zomwe akatswiri a masamu azitulukira posachedwapa mu 1999?

MFUNDO ZOTHANDIZA MABANJA

Kodi Mungatani Kuti Muziugwira Mtima?

Mfundo 5 zokuthandizani kuti muziugwira mtima.

ANTHU NDI MAYIKO

Dziko la Costa Rica

Werengani nkhaniyi kuti mudziwe chifukwa chake anthu a m’dzikoli amadziwika kuti Atiko.

KUCHEZA NDI ANTHU

“Ndimayesetsa Kuti Ndisamangoganizira za Matenda Anga”

N’chiyani chimathandiza Elisa kupirira komanso kuiwalako matenda ake?

ZIMENE BAIBULO LIMANENA

Mavuto

Kodi Mulungu amamva bwanji tikamavutika?

ZOCHITIKA PADZIKOLI

Nkhani Zokhudza Zipembedzo

Nkhani zaposachedwapa zikusonyeza kuti zipembedzo zalephera kugwirizanitsa anthu.

Zina zimene zili pawebusaiti

N’chifukwa Chiyani Ndiyenera Kupewa Kuonerera Zolaula?

Kodi kuonera zolaula n’kofanana motani ndi kusuta fodya?

Uzikhala Wokoma Mtima Ndiponso Wopatsa

Onerani kuti mudziwe mmene Kalebe ndi Sofiya amasangalalira akamagawana zinthu.