Pitani ku nkhani yake

Pitani ku mitu ya nkhani

Buku la Malaki

Machaputala

1 2 3 4

Mitu

  • 1

    • Yehova amakonda anthu ake (1-5)

    • Ansembe ankapereka nsembe zosalongosoka (6-14)

      • Dzina la Mulungu lidzakhala lalikulu pakati pa anthu a mitundu ina (11)

  • 2

    • Ansembe ankalephera kulangiza anthu (1-9)

      • Ansembe ankayenera kuphunzitsa anthu za Mulungu (7)

    • Anthu ankathetsa mabanja pa zifukwa zosamveka (10-17)

      • “‘Ndimadana ndi zoti anthu azithetsa mabanja,’ watero Yehova” (16)

  • 3

    • Ambuye woona anabwera kudzayeretsa kachisi (1-5)

      • Mthenga wa pangano (1)

    • Anawalimbikitsa kuti abwerere kwa Yehova (6-12)

      • Yehova sasintha (6)

      • “Bwererani kwa ine ndipo ine ndidzabwerera kwa inu” (7)

      • ‘Bweretsani chakhumi chonse ndipo Yehova adzakudalitsani’ (10)

    • Anthu olungama ndiponso anthu oipa (13-18)

      • Buku la chikumbutso linalembedwa pamaso pa Mulungu (16)

      • Kusiyana pakati pa wolungama ndi woipa (18)

  • 4

    • Eliya adzabwera tsiku la Yehova lisanafike (1-6)

      • ‘Dzuwa la chilungamo lidzawala’ (2)