Pitani ku nkhani yake

Zimene Achinyamata Amafunsa

 

Anzanu

N’chifukwa Chiyani Anzanga Sandikonda?

Si inu nokha amene mukusowa wocheza naye kapena amene mulibe mnzanu. Werengani nkhaniyi kuti muone mmene anthu ena athetsera vutoli.

Mungatani Kuti Musamachite Manyazi Kwambiri?

Zinthu zisamakupiteni ndipo mukhoza kupeza anzanu ambiri.

Kodi Ndiwonjezere Anzanga?

Zimakhala bwino kukhala ndi kagulu kochepa ka anzanu, koma sikuti zimenezi zimathandiza nthawi zonse. N’chifukwa chiyani?

Kodi Ndingakulitse Bwanji Luso Lolankhulana Ndi Anthu?

Mfundo zitatu zimene zingakuthandizeni kuti musamavutike kuyamba kulakhulana ndi anthu.

Kodi Ndi Mnzanga Chabe Kapena Amandifuna?—Gawo 2: Kodi Ndikumukopa?

Kodi mnzanuyu angaganize kuti mukumufuna chibwenzi? Zimene zingakuthandizeni.

Ndingatani Ngati Mnzanga Atandikhumudwitsa?

Muzikumbukira kuti tonse timakhumudwitsa anzathu. Koma kodi mungatani ngati mnzanu atalankhula kapena kuchita zinthu zomwe zakukhumudwitsani?

Ndingatani Ngati Anzanga Amandiona Kuti Ndine Wotsalira?

Kodi mumaona kuti n’zoyenera kuchita zinthu kuti mufanane ndi anzanu omwe satsatira mfundo za makhalidwe abwino kapena mumaona kuti chofunika ndi kungokhala mmene mulili?

N’chifukwa Chiyani Ndimangolankhula Zolakwika?

Kodi n’chiyani chingakuthandizeni kuti muziganiza musanalankhule?

Kodi Ndingatani Ngati Anthu Ena Akukonda Kunena za Ine?

Kodi mungatani kuti zinthu zabodza zimene anthu akufalitsa zokhudza inuyo zisawononge mbiri yanu?

Kodi Kukopana Kuli Ndi Vuto?

Kodi kukopana n’kutani? N’chifukwa chiyani anthu ena amakopana? Kodi kukopana kuli ndi vuto?

Kodi Ndiyenera Kudziwa Zotani Zokhudza Mameseji a Pafoni?

Mameseji a pafoni akhoza kuononga ubwenzi wanu ndi anzanu komanso mbiri yanu. Werengani kuti mudziwe mmene zimenezi zingachitikire

Mabanja

Kodi Ndingatani Kuti Ndizigwirizana ndi Makolo Anga?

Onani zinthu 5 zimene mungachite kuti musamakangane ndi makolo anu.

Kodi Ndingakambirane Bwanji ndi Makolo Anga za Malamulo Amene Anakhazikitsa?

Mukamalankhula mwaulemu ndi makolo anu zinthu zingakuyendereni bwino.

Kodi N’zofunikadi Kuti Makolo Azikhazikitsa Malamulo Oti Muzitsatira?

Kodi mumaona kuti malamulo amene makolo anu anakhazikitsa ndi ovuta? M’nkhaniyi muli mfundo zimene zingakuthandizeni kuti muzitha kuona malamulowo moyenera.

Kodi Ndingatani Ngati Sindinamvere Lamulo la Makolo Anga??

Simungasinthe zimene zachitika koma mungathandize kuti zinthu zisaipe kwambiri. Nkhaniyi ikufotokoza zimene mungachite.

Kodi Ndingatani Kuti Makolo Anga Azindikhulupirira?

Kuphunzira kukhala wodalirika ndi kofunika kwa aliyense osati kwa achinyamata okha.

Kodi Mumaona Kuti Makolo Anu Sangakuloleni Kupita Kokasangalala?

Kodi ndingozemba n’kupita kokasangalala, kapena ndipemphe makolo anga?

Kodi Ndingatani Ngati Bambo Kapena Mayi Anga Atayamba Kudwala?

Si inu nokha amene mukukumana ndi vuto limeneli. Werengani nkhaniyi kuti mudziwe zimene atsikana ena awiri anachita kuti athe kupirira.

Kodi Makolo Anu Akufuna Kuthetsa Banja Lawo?

Kodi mungatani kuti musamangokhala wokhumudwa kapena wokwiya?

N’chifukwa Chiyani Ndiyenera Kukhala Mwamtendere ndi Abale Anga?

Ngakhale kuti mumakonda abale anu, koma nthawi zina mukhoza kuwakhumudwitsa.

Kodi Ndingatani Kuti Ndizikhala ndi Mpata Womachita Zinthu Pandekha?

Kodi mumaona kuti makolo anu akukulondalondani? Nanga mungatani kuti vuto limeneli lichepe?

Kodi Ndafika Poti Nditha Kuchoka Pakhomo pa Makolo Anga?

Kodi mungadzifunse mafunso ati musanaganize zoti musamuke?

Technology

Kodi Ndiyenera Kudziwa Zotani Zokhudza Kusewera Magemu a Pazipangizo Zamakono?

Mwina simunaganizirepo ubwino komanso kuipa kosewera magemu.

Kodi Ndiyenera Kudziwa Zotani Zokhudza Mameseji a Pafoni?

Mameseji a pafoni akhoza kuononga ubwenzi wanu ndi anzanu komanso mbiri yanu. Werengani kuti mudziwe mmene zimenezi zingachitikire

Kodi Kukhala Munthu Wotchuka pa Intaneti Kuli Ndi Phindu?

Anthu ena amalolera kuika moyo wawo pangozi n’cholinga choti akhale ndi anthu ambiri owatsatira komanso okonda zimene aposita pa intaneti. Kodi kukhala wotchuka pa intaneti n’kothandizadi?

Kodi Malo Ochezera a pa Intaneti Akusokoneza Moyo Wanga?

Malo ochezera a pa intaneti amakomedwetsa. Mfundo zotsatirazi zikuthandizani kuti muzidziletsa.

Kodi Ndiyenera Kudziwa Zotani pa Nkhani Yotumizirana Zithunzi pa Intaneti?

Kuika zinthu zimene zimakusangalatsani pa intaneti ndi njira yabwino yolumikizirana ndi anzanu komanso anthu a m’banja lanu, koma kukhoza kukhalanso koopsa.

Ndingatani Ngati Anthu Ena Amandivutitsa pa Intaneti?

Zimene muyenera kuchita komanso zimene mungachite kuti mudziteteze.

Kodi Ndi Bwino Kumachita Zinthu Zingapo Nthawi Imodzi?

Kodi mungathedi kumachita zinthu zina nthawi imodzi popanda kusokonezeka?

Kodi Ndingatani Kuti Maganizo Anga Azikhala pa Zimene Ndikupanga?

Taganizirani njira zitatu zosonyeza mmene zipangizo zamakono zingakusokonezereni ndipo onani zimene mungachite kuti muzikwanitsa kuika maganizo anu pa chinthu chimodzi.

Kodi Ndiyenera Kudziwa Zotani pa Nkhani Yotumizirana Mameseji ndi Zinthu Zina Zolaula?

Kodi munthu wina amakukakamizani kuti mumutumizire zolaula? Kodi kutumizirana zolaula kuli ndi mavuto otani? Kodi ndi kukopana basi?

Ndingatani Ngati Makolo Anga Sakundilola Kugwiritsa Ntchito Malo Ochezera a pa Intaneti?

Zikuoneka ngati aliyense amagwiritsa ntchito malo ochezera a pa intaneti, koma kodi zimenezi n’zoona? Kodi mungatani ngati makolo anu samakulolani kugwiritsa ntchito malowa?

Sukulu

Kodi Ndingatani Kuti Ndizigwirizana Ndi Aphunzitsi Anga?

Ngati mphunzitsi wanu ndi wovuta, simufunika kusiya sukulu, m’malomwake pali mfundo zimene zingakuthandizeni kuti moyo musaumve kuwawa. Tayesani kuchita zotsatirazi.

Ndingatani Kuti Ndimalize Homuweki Yanga?

Ngati mukulephera kumaliza homuweki yanu, simukufunika kuchita kudzipanikiza. Koma mukungofunika kumachita zinthu mwadongosolo.

Kodi Ndingatani Kuti Ndizipindula ndi Sukulu Ngakhale Pamene Ndikuphunzirira Kunyumba?

Ana asukulu ambiri ayamba kuphunzirira kunyumba. Pali mfundo 5 zomwe zingakuthandizeni kuti muzipindula ndi maphunziro pamene mwasiya kaye kupita kusukulu.

Kodi Sukulu Yakutopetsani?

Kodi aphunzitsi anu ndi otopetsa? Kodi mukamaphunzira maphunziro enaake mumangoona ngati mukutaya nthawi?

Ndingatani Ngati Ndimalephera ku Sukulu?

Musanaganize zosiya kulimbikira kusukulu, ganizirani mfundo 6 zomwe zingakuthandizeni kuti muzikhoza m’kalasi.

Kodi Ndisiye Sukulu?

Pali zambiri zimene munthu ayenera kuganizira poyankha funsoli.

Kodi Ndingatani Anthu Ena Akamandivutitsa?

Anthu ambiri amene akuvutitsidwa amaona kuti palibe chimene angachite. Nkhaniyi ikufotokoza zimene mungachite kuti anthu asiye kukuvutitsani.

N’chifukwa Chiyani Muyenera Kuphunzira Chinenero China?

Kodi pamakhala mavuto otani? Nanga pamakhala mapindu otani?

Kodi Zinthu Zinachita Kulengedwa?—Gawo 1: N’chifukwa Chiyani Ndimakhulupirira Kuti Kuli Mulungu?

Kodi mungakonde kuti muzifotokozera ena molimba mtima zimene mumakhulupirira zoti kuli Mulungu? Werengani nkhaniyi kuti mupeze mfundo zimene zingakuthandizeni kuyankha ngati munthu wina wakufunsani zimene mumakhulupirira.

Kodi Zinthu Zinachita Kulengedwa?—Gawo 3: N’chifukwa Chiyani Ndiyenera Kukhulupirira Kuti Zinthu Zinachita Kulengedwa?

Kodi munthu amafunika kudana ndi sayansi n’cholinga choti azikhulupirira zoti zinthu zinachita kulengedwa?

Kodi Zinthu Zinachita Kulengedwa?—Gawo 4: Kodi Ndingafotokozere Bwanji Munthu Kuti Zinthu Zinachita Kulengedwa?

Simukufunika kuchita kukhala wodziwa kwambiri sayansi kuti muthe kufotokozera munthu umboni wosonyeza kuti n’zomveka kukhulupirira kuti zinthu zinachita kulengedwa. Gwiritsirani ntchito zitsanzo zosavuta kumva zopezeka m’Baibulo.

Life Skills

Kodi Ndingatani Kuti Ndisamasinthesinthe Mmene Ndimamvera?

Anthu ambiri amasinthasintha mmene akumvera, koma zimenezi zimasokoneza ana ambiri. Koma chosangalatsa n’choti utha kudziwa bwino zimene zikukuchitikira komanso n’zotheka kupirira vutoli.

Kodi Ndingatani Kuti Ndisamangoganizira Zinthu Zolakwika?

Mukhoza kumaganizira zinthu zabwino mukamatsatira mfundo zomwe zili mu nkhaniyi.

Kodi Ndingatani Kuti Ndisamapse Mtima?

Pali malemba 5 amene angakuthandizeni kuti musamapse mtima wina akakuyambani.

N’chiyani Chingandithandize Ndikakhala Ndi Nkhawa?

Zinthu 5 zimene zingakuthandizeni kuti muzida nkhawa pa zinthu zoyenera m’malo mwa zinthu zimene zingakubweretserani mavuto.

Kodi N’chiyani Chingandithandize Ndikakumana ndi Mavuto?

Achinyamata akufotokoza zimene anachita atakumana ndi mavuto.

Kodi Ndingatani Kuti Ndisamagonje Poyesedwa?

Onani zinthu zitatu zimene zingakuthandizeni kuti musamagonje mukayesedwa.

Ndingatani Kuti Ndizigawa Bwino Nthawi Yanga?

Mfundo 5 zomwe zingakuthandizeni kuti muzipewa kuwononga nthawi yanu.

Kodi Ineyo Ndingatani Kuti Ndipewe Vuto la Kupanikizika?

Kodi n’chiyani chimayambitsa vuto la kupanikizika? Kodi inunso mumapanikizika kwambiri? Ngati ndi choncho, kodi mungatani kuti muthane ndi vutoli?

Kodi Ndingatani Kuti Ndisamachite Zinthu Mozengereza?

Werengani malangizo amene angakuthandizeni kuti musamachite zinthu mozengereza

Kodi Ndingatani Kuti Ndisamawononge Ndalama?

Kodi nthawi ina munapitapo mu shopu kuti mukangoona zinthu koma n’kugula chinthu chodula kwambiri? Ngati ndi choncho, nkhaniyi ikuthandizani.

Kodi Ndizitani Ndikalakwitsa Zinazake?

Aliyense amalakwitsa koma si onse amene amaphunzirapo kanthu.

Kodi Ndizitani Munthu Wina Akandidzudzula?

Achinyamata ena amakhala ngati tambula yagalasi yomwe sichedwa kusweka moti akangodzudzulidwa ngakhale pa zinthu zazing’ono, amakwiya kwambiri. Kodi inunso mumatero?

N’chifukwa Chiyani Tiyenera Kupewa Kunama ndiponso Kuba?

Kodi si zoona kuti anthu achinyengo zinthu zimawayendera bwino?

Kodi Ndine Munthu Wodalirika?

Achinyamata ena amapatsidwa ufulu wambiri poyerekezera ndi anzawo ena. Kodi n’chiyani chimachititsa kuti pakhale kusiyana kotereku?

Kodi Ndine Wopirira?

Aliyense amakumana ndi mavuto, choncho m’pofunika kuphunzira kukhala wopirira, ngakhale mavutowo atakhala aang’ono kapena aakulu.

Kodi Ndingatani Kuti Maganizo Anga Azikhala pa Zimene Ndikupanga?

Taganizirani njira zitatu zosonyeza mmene zipangizo zamakono zingakusokonezereni ndipo onani zimene mungachite kuti muzikwanitsa kuika maganizo anu pa chinthu chimodzi.

N’chifukwa Chiyani Muyenera Kuphunzira Chinenero China?

Kodi pamakhala mavuto otani? Nanga pamakhala mapindu otani?

Kodi Ndafika Poti Nditha Kuchoka Pakhomo pa Makolo Anga?

Kodi mungadzifunse mafunso ati musanaganize zoti musamuke?

Mungatani Kuti Musamachite Manyazi Kwambiri?

Zinthu zisamakupiteni ndipo mukhoza kupeza anzanu ambiri.

Ndingatani Ngati Anzanga Amandiona Kuti Ndine Wotsalira?

Kodi mumaona kuti n’zoyenera kuchita zinthu kuti mufanane ndi anzanu omwe satsatira mfundo za makhalidwe abwino kapena mumaona kuti chofunika ndi kungokhala mmene mulili?

Kodi Kukhala ndi Ulemu N’kofunikadi?

Kodi ulemu ndi wofunika masiku ano, kapena ndi nkhani yachikale?

N’chifukwa Chiyani Ndimangolankhula Zolakwika?

Kodi n’chiyani chingakuthandizeni kuti muziganiza musanalankhule?

N’chifukwa Chiyani Ndiyenera Kupepesa?

Onani zifukwa zitatu zimene muyenera kupepesera ngakhale pamene mukuona kuti simunalakwe chilichonse.

N’chifukwa Chiyani Ndikufunika Kumathandiza Ena?

Kuchitira ena zabwino kumakuthandizani m’njira ziwiri. Kodi njira zimenezi ndi zotani?

Kodi Ndingatani Ngati Anthu Ena Akukonda Kunena za Ine?

Kodi mungatani kuti zinthu zabodza zimene anthu akufalitsa zokhudza inuyo zisawononge mbiri yanu?

Ndingatani Ngati Mnzanga Atandikhumudwitsa?

Muzikumbukira kuti tonse timakhumudwitsa anzathu. Koma kodi mungatani ngati mnzanu atalankhula kapena kuchita zinthu zomwe zakukhumudwitsani?

Kodi Ndingatani Anthu Ena Akamandivutitsa?

Anthu ambiri amene akuvutitsidwa amaona kuti palibe chimene angachite. Nkhaniyi ikufotokoza zimene mungachite kuti anthu asiye kukuvutitsani.

Kudziwa Mmene Mulili

N’chifukwa Chiyani Sindikuyenera Kutsanzira Khalidwe la Anthu Omwe Amaonetsedwa M’mafilimu, pa TV ndi M’magazini?​—Gawo 1: Ya Atsikana

Achinyamata ambiri amaganiza kuti akuchita zinthu m’njira yawoyawo, koma amakhala akungotsanzira zochita za ena.

N’chifukwa Chiyani Sindikuyenera Kutsanzira Khalidwe la Anthu Omwe Amaonetsedwa M’mafilimu, pa TV ndi M’magazini?​—Gawo 2: Ya Anyamata

Kodi kutsanzira makhalidwe a anthu amene amasonyezedwa m’mafilimu, pa TV ndi m’magazini kungapangitse kuti anthu asamakopeke nanu?

Kodi Ndine Munthu Wodalirika?

Achinyamata ena amapatsidwa ufulu wambiri poyerekezera ndi anzawo ena. Kodi n’chiyani chimachititsa kuti pakhale kusiyana kotereku?

Kodi Ndingakulitse Bwanji Luso Lolankhulana Ndi Anthu?

Mfundo zitatu zimene zingakuthandizeni kuti musamavutike kuyamba kulakhulana ndi anthu.

N’chifukwa Chiyani Tiyenera Kupewa Kunama ndiponso Kuba?

Kodi si zoona kuti anthu achinyengo zinthu zimawayendera bwino?

Kodi Ndine Wopirira?

Aliyense amakumana ndi mavuto, choncho m’pofunika kuphunzira kukhala wopirira, ngakhale mavutowo atakhala aang’ono kapena aakulu.

Kodi Ndizitani Munthu Wina Akandidzudzula?

Achinyamata ena amakhala ngati tambula yagalasi yomwe sichedwa kusweka moti akangodzudzulidwa ngakhale pa zinthu zazing’ono, amakwiya kwambiri. Kodi inunso mumatero?

Kodi Ndingaphunzitse Bwanji Chikumbumtima Changa?

Chikumbumtima chanu chimasonyeza kuti ndinu munthu wotani. Chimasonyezanso mfundo zimene mumakhulupirira. Ndiye kodi chikumbumtima chanu chimasonyeza zotani zokhudza inuyo?

Kodi Ndimafuna Kuti Ndisamalakwitse Chilichonse?

Kodi mungasiyanitse bwanji pakati pa kuyesetsa kuchita bwino ndi kuyesa kuchita zinthu zosatheka?

Kodi Kukhala Munthu Wotchuka pa Intaneti Kuli Ndi Phindu?

Anthu ena amalolera kuika moyo wawo pangozi n’cholinga choti akhale ndi anthu ambiri owatsatira komanso okonda zimene aposita pa intaneti. Kodi kukhala wotchuka pa intaneti n’kothandizadi?

Kodi Ndingatani Kuti Ndisiye Kukhala Moyo Wachiphamaso?

Njira 4 zomwe zingakuthandizeni kuti musiye kukhala moyo wachinyengowu.

Kodi Ndingasankhe Bwanji Munthu Wabwino Woti Ndizimutsanzira?

Kukhala ndi munthu woti muzimutsanzira kungakuthandizeni kupewa mavuto, kukwaniritsa zolinga zanu komanso kuti zinthu zizikuyenderani bwino. Kodi inuyo muyenera kutsanzira munthu wotani?

N’chifukwa Chiyani Ndikufunika Kumathandiza Ena?

Kuchitira ena zabwino kumakuthandizani m’njira ziwiri. Kodi njira zimenezi ndi zotani?

Kodi Ndizitani Ndikalakwitsa Zinazake?

Aliyense amalakwitsa koma si onse amene amaphunzirapo kanthu.

Kodi Ndingatani Kuti Ndisamagonje Poyesedwa?

Onani zinthu zitatu zimene zingakuthandizeni kuti musamagonje mukayesedwa.

Kodi Ndimakonda Kuvala Zovala Zotani?

Werengani nkhaniyi kuti mudziwe zokhudza maganizo olakwika amene anthu amakhala nawo pa nkhani ya mafasho.

Kodi Ndimangokhalira Kuganizira za Maonekedwe Anga?

Kodi mungatani kuti muzisangalala ndi mmene mumaonekera?

Kodi Palibe Vuto Ngati Nditadzilemba Pathupi Langa?

N’chiyani chingakuthandizeni kuti musankhe mwanzeru pa nkhani imeneyi?

Bad Habits

Kodi Kutukwana N’koipadi?

Popeza kuti anthu ambiri amatukwana, kodi tinganene kuti n’koipadi?

N’chifukwa Chiyani Ndiyenera Kupewa Kuonerera Zolaula?

Kodi kuonera zolaula n’kofanana motani ndi kusuta fodya?

Kodi Mukulephera Kusiya Kuonerera Zinthu Zolaula?

Baibulo lingakuthandizeni kuti mumvetse cholinga cha zinthu zolaula.

Kodi Ndingatani Kuti Ndisamagonje Poyesedwa?

Onani zinthu zitatu zimene zingakuthandizeni kuti musamagonje mukayesedwa.

Kodi Ndi Bwino Kumachita Zinthu Zingapo Nthawi Imodzi?

Kodi mungathedi kumachita zinthu zina nthawi imodzi popanda kusokonezeka?

Kodi Ndingatani Kuti Ndisamachite Zinthu Mozengereza?

Werengani malangizo amene angakuthandizeni kuti musamachite zinthu mozengereza

Free Time

Kodi Palibe Vuto Ngati Nditamangomvera Nyimbo Iliyonse?

Popeza nyimbo ndi zamphamvu, nkhaniyi ingakuthandizeni kudziwa zimene mungachite kuti muzisankha nyimbo mwanzeru.

Kodi Ndiyenera Kudziwa Zotani Zokhudza Kusewera Magemu a Pazipangizo Zamakono?

Mwina simunaganizirepo ubwino komanso kuipa kosewera magemu.

Kodi Ndiyenera Kuganizira Mfundo Ziti pa Nkhani ya Masewera?

Muyenera kuganizira masewera amene mumachita, zimene mumachita posewerapo ndiponso kuchuluka kwa nthawi imene mumachita masewerawo.

Ndingatani Kuti Ndizigawa Bwino Nthawi Yanga?

Mfundo 5 zomwe zingakuthandizeni kuti muzipewa kuwononga nthawi yanu.

Ndingatani Ngati Ndaboweka?

Kodi zipangizo zamakono zingakuthandizeni pa nkhaniyi? Nanga kodi zinthu zingamakuyendereni potengera mmene mumaonera zinthu?

Kodi Kuchita Zamatsenga Kuli ndi Vuto Lililonse?

Anthu ambiri masiku ano amachita chidwi ndi zamatsenga, ziwanda, mavampaya, mizukwa ndi ufiti. Kodi pali vuto lililonse ndi zinthu zimenezi?

Kodi Mumaona Kuti Makolo Anu Sangakuloleni Kupita Kokasangalala?

Kodi ndingozemba n’kupita kokasangalala, kapena ndipemphe makolo anga?

Kugonana

Kodi Ndizitani Ngati Ena Akundichitira Zachipongwe?

Werengani nkhaniyi kuti mudziwe tanthauzo la kuchitiridwa zachipongwe komanso zimene mungachite ngati mutachitiridwa zachipongwezo.

Kodi Ndiyenera Kudziwa Zotani Zokhudza Nkhanza za Kugonana?—Gawo 1: Mmene Mungadzitetezere

Pali njira zitatu zimene zingakuthandizeni kuti mupewe kuchitidwa nkhanza zokhudza kugonana.

Kodi Ndiyenera Kudziwa Zotani Zokhudza Nkhanza za Kugonana?​—Gawo 2: Zimene Mungachite Ngati Munachitidwapo Nkhanza Zotere

Werengani zimene zinathandiza anthu omwe anachitidwa nkhanza zokhudza kugonana kuti azikhala osangalala.

Kodi Ndingafotokoze Bwanji Zimene Ndimakhulupirira pa Nkhani ya Kugonana?

Ngati mutafunsidwa kuti: ‘Kodi sunagonanepo ndi munthu chibadwire?’ kodi mungathe kugwiritsa ntchito Baibulo poyankha?

Kodi Kugonana M’kamwa Kumakhaladi Kugonana?

Kodi mtsikana akhoza kutenga mimba chifukwa chogonana m’kamwa?

Kodi Kugonana Kwa Amuna Kapena Akazi Okhaokha N’kolakwika?

Kodi Baibulo limanena kuti anthu amene amagonana ndi amuna kapena akazi anzawo ndi oipa? Kodi Mkhristu akhoza kukhala paubwenzi ndi Mulungu ngakhale atamakhala ndi chilakolako chofuna kugonana ndi amuna kapena akazi anzake?

Ndingatani Ngati Anzanga Akundikakamiza Kugonana?

Onani zimene anthu ena amakhulupirira komanso zoona zake pa nkhani ya kugonana. Nkhaniyi ikuthandizani kuti musankhe zinthu mwanzeru.

Ndingatani Kuti Ndisamangoganizira Zogonana?

Kodi mungatsatire mfundo ziti ngati mutayamba kuganizira zogonana?

Kodi ndi Bwino Kulonjeza Kuti Ndikhala Wodzisunga Mpaka Ndidzalowe M’banja?

Kodi kuchita zimenezi kungathandizedi kupewa zogonana musanalowe m’banja?

Kodi Ndiyenera Kudziwa Zotani pa Nkhani Yotumizirana Mameseji ndi Zinthu Zina Zolaula?

Kodi munthu wina amakukakamizani kuti mumutumizire zolaula? Kodi kutumizirana zolaula kuli ndi mavuto otani? Kodi ndi kukopana basi?

N’chifukwa Chiyani Ndiyenera Kupewa Kuonerera Zolaula?

Kodi kuonera zolaula n’kofanana motani ndi kusuta fodya?

Kodi Mukulephera Kusiya Kuonerera Zinthu Zolaula?

Baibulo lingakuthandizeni kuti mumvetse cholinga cha zinthu zolaula.

Kodi Ndingatani Kuti Ndisamagonje Poyesedwa?

Onani zinthu zitatu zimene zingakuthandizeni kuti musamagonje mukayesedwa.

Kukhala pa Chibwenzi

Kodi Ndine Wokonzeka Kukhala Pachibwenzi?

Mfundo 5 zimene zingakuthandizeni kudziwa ngati muli wokonzeka kukhala pachibwenzi komanso kulowa m’banja

Kodi Kukopana Kuli Ndi Vuto?

Kodi kukopana n’kutani? N’chifukwa chiyani anthu ena amakopana? Kodi kukopana kuli ndi vuto?

Kodi Ndi Mnzanga Chabe Kapena Amandifuna?​—Gawo 1: Kodi Ndikuona Zizindikiro Zotani?

Nkhaniyi ingakuthandizeni kuti mudziwe ngati munthu amakukondani kapena akungofuna kukhala mnzanu chabe.

Kodi Ndi Mnzanga Chabe Kapena Amandifuna?—Gawo 2: Kodi Ndikumukopa?

Kodi mnzanuyu angaganize kuti mukumufuna chibwenzi? Zimene zingakuthandizeni.

Kodi Ndingatani Ngati Chibwenzi Chatha?

Werengani nkhaniyi kuti mudziwe zimene mungachite ngati mwakhumudwa chifukwa chakuti chibwenzi chatha.

Physical Health

Kodi Ndingatani Ngati Ndikudwala Matenda Aakulu? (Gawo 1)

Achinyamata 4 akufotokoza zimene zikuwathandiza kupirira matenda awo kuti asamangokhalira kudandaula.

Kodi Ndingatani Ngati Ndikudwala Matenda Aakulu?—Gawo 2

Werengani zimene achinyamata ena anachita kuti athe kupirira matenda aakulu komanso kuti azikhalabe osangalala.

Kodi Ndingatani Ngati Ndikudwala Matenda Aakulu?—Gawo 3

Zitsanzo za achinyamata atatu zingakuthandizeni kupirira matenda.

Zimene Zingakuthandizeni Mukatha Msinkhu

Werengani kuti mudziwe zimene zimachitika pa nthawiyi komanso zimene zingakuthandizeni.

Kodi Ineyo Ndingatani Kuti Ndipewe Vuto la Kupanikizika?

Kodi n’chiyani chimayambitsa vuto la kupanikizika? Kodi inunso mumapanikizika kwambiri? Ngati ndi choncho, kodi mungatani kuti muthane ndi vutoli?

Kodi Ndiyenera Kudziwa Chiyani pa Nkhani Yomwa Mowa?

Onani mmene mungapewere kuphwanya malamulo, kuononga mbiri yanu, kuchitidwa nkhanza zokhudza kugonana, kukonda kwambiri mowa komanso imfa.

Zomwe Ndiyenera Kudziwa pa Nkhani Yosuta Kapena Kuvepa

Zinthu zimene anthu otchuka kapena anzako amaziona ngati ‘zosangalatsa’ sizikhala zosangalatsa kwenikweni koma amakhala akudziputira mavuto aakulu. Dziwani mavuto amene amabwera chifukwa cha kuvepa komanso mmene mungawapewere.

Kodi Ndingatani Kuti Ndizigona Mokwanira?

Mfundo 7 zimene zingakuthandizeni kuti muzigona mokwanira.

Ndingatani Kuti Ndizikonda Masewera Olimbitsa Thupi?

Kuwonjezera pa kukhala ndi thanzi labwino, kodi masewera olimbitsa thupi angakuthandizeninso bwanji?

Kodi Ndingatani Kuti Ndizidya Zakudya Zopatsa Thanzi?

Munthu amene sadya zakudya zopatsa thanzi ali wamng’ono amachitanso zomwezo akadzakula. Choncho ndibwino kuti muzikhala ndi chizolowezi chomadya zakudya zopatsa thanzi panopa.

Ndingatani Kuti Ndichepetse Thupi?

Ngati mukufuna kuchepetsa thupi si bwino kumasala zakudya zina, mukhoza kungosintha zinthu zina pa moyo wanu.

Emotional Health

Kodi Ndingatani Kuti Ndisamasinthesinthe Mmene Ndimamvera?

Anthu ambiri amasinthasintha mmene akumvera, koma zimenezi zimasokoneza ana ambiri. Koma chosangalatsa n’choti utha kudziwa bwino zimene zikukuchitikira komanso n’zotheka kupirira vutoli.

Kodi Ndingatani Kuti Ndisamangoganizira Zinthu Zolakwika?

Mukhoza kumaganizira zinthu zabwino mukamatsatira mfundo zomwe zili mu nkhaniyi.

Kodi Ndingatani Ngati Ndili ndi Matenda Ovutika Maganizo?

Mfundo zomwe zili m’nkhaniyi zingakuthandizeni kudziwa zimene mungachite kuti muchire.

N’chiyani Chingandithandize Ndikakhala Ndi Nkhawa?

Zinthu 5 zimene zingakuthandizeni kuti muzida nkhawa pa zinthu zoyenera m’malo mwa zinthu zimene zingakubweretserani mavuto.

Kodi Ndingatani Kuti Ndisamapse Mtima?

Pali malemba 5 amene angakuthandizeni kuti musamapse mtima wina akakuyambani.

Kodi Ndimafuna Kuti Ndisamalakwitse Chilichonse?

Kodi mungasiyanitse bwanji pakati pa kuyesetsa kuchita bwino ndi kuyesa kuchita zinthu zosatheka?

Kodi Ndine Wopirira?

Aliyense amakumana ndi mavuto, choncho m’pofunika kuphunzira kukhala wopirira, ngakhale mavutowo atakhala aang’ono kapena aakulu.

Kodi N’chiyani Chingandithandize Ndikakumana ndi Mavuto?

Achinyamata akufotokoza zimene anachita atakumana ndi mavuto.

Ndingatani Ngati Ndili Ndi Maganizo Ofuna Kudzipha?

Zinthu 4 zomwe zingakuthandizeni ngati muli ndi maganizo oona kuti bola kungofa.

Kodi Ndingatani Anthu Ena Akamandivutitsa?

Anthu ambiri amene akuvutitsidwa amaona kuti palibe chimene angachite. Nkhaniyi ikufotokoza zimene mungachite kuti anthu asiye kukuvutitsani.

Ndingatani Ngati Anthu Ena Amandivutitsa pa Intaneti?

Zimene muyenera kuchita komanso zimene mungachite kuti mudziteteze.

Kodi Malo Ochezera a pa Intaneti Akusokoneza Moyo Wanga?

Malo ochezera a pa intaneti amakomedwetsa. Mfundo zotsatirazi zikuthandizani kuti muzidziletsa.

Zimene Zingakuthandizeni Mukatha Msinkhu

Werengani kuti mudziwe zimene zimachitika pa nthawiyi komanso zimene zingakuthandizeni.

N’chifukwa Chiyani Ndimadzivulaza?

Achinyamata ena ali ndi vuto lodzivulaza mwadala. Ngati muli ndi khalidwe limeneli, kodi mungatani kuti mulisiye?

Kodi Ineyo Ndingatani Kuti Ndipewe Vuto la Kupanikizika?

Kodi n’chiyani chimayambitsa vuto la kupanikizika? Kodi inunso mumapanikizika kwambiri? Ngati ndi choncho, kodi mungatani kuti muthane ndi vutoli?

Kodi Ndiyenera Kudziwa Zotani Zokhudza Nkhanza za Kugonana?​—Gawo 2: Zimene Mungachite Ngati Munachitidwapo Nkhanza Zotere

Werengani zimene zinathandiza anthu omwe anachitidwa nkhanza zokhudza kugonana kuti azikhala osangalala.

Ubwenzi ndi Mulungu

Kodi Zinthu Zinachita Kulengedwa?—Gawo 1: N’chifukwa Chiyani Ndimakhulupirira Kuti Kuli Mulungu?

Kodi mungakonde kuti muzifotokozera ena molimba mtima zimene mumakhulupirira zoti kuli Mulungu? Werengani nkhaniyi kuti mupeze mfundo zimene zingakuthandizeni kuyankha ngati munthu wina wakufunsani zimene mumakhulupirira.

Kodi Zinthu Zinachita Kulengedwa?—Gawo 3: N’chifukwa Chiyani Ndiyenera Kukhulupirira Kuti Zinthu Zinachita Kulengedwa?

Kodi munthu amafunika kudana ndi sayansi n’cholinga choti azikhulupirira zoti zinthu zinachita kulengedwa?

Kodi Zinthu Zinachita Kulengedwa?—Gawo 4: Kodi Ndingafotokozere Bwanji Munthu Kuti Zinthu Zinachita Kulengedwa?

Simukufunika kuchita kukhala wodziwa kwambiri sayansi kuti muthe kufotokozera munthu umboni wosonyeza kuti n’zomveka kukhulupirira kuti zinthu zinachita kulengedwa. Gwiritsirani ntchito zitsanzo zosavuta kumva zopezeka m’Baibulo.

N’chifukwa Chiyani Ndiyenera Kupemphera?

Kodi pemphero limangothandiza kuti maganizo akhale m’malo, kapena limathandizanso m’njira zina?

N’chifukwa Chiyani Ndiyenera Kupezeka Pamisonkhano ya pa Nyumba ya Ufumu?

Mlungu uliwonse a Mboni za Yehova amakumana kawiri pa nyumba yomwe amalambirira yotchedwa Nyumba ya Ufumu. Kodi kumeneko kumachitika zotani, nanga mungapindule bwanji ngati mutapezeka pamisonkhano yawo?

Kodi Ndingatani Kuti Ndisiye Kukhala Moyo Wachiphamaso?

Njira 4 zomwe zingakuthandizeni kuti musiye kukhala moyo wachinyengowu.

Kodi Baibulo Lingandithandize Bwanji?—Gawo 1: Kuganizira Mozama Mfundo za M’baibulo

Tiyerekeze kuti mwaona chikwama cha ndalama chomwe chikuoneka kuti ndi chakalekale, kodi simungakhale ndi chidwi kuti muone zimene zili mkatimo? Baibulo lili ngati chikwama choterocho. Mumapezeka mfundo zambiri zothandiza.

Kodi Baibulo Lingandithandize Bwanji?—Gawo 2: Zimene Mungachite Kuti Kuwerenga Baibulo Kuzikusangalatsani

Zinthu 5 zomwe zingakuthandizeni kuti muziona zimene mukuwerenga m’Baibulo kuti ndi zenizeni.

Kodi Baibulo Lingandithandize Bwanji?—Gawo 3: Zimene Mungachite Kuti Kuwerenga Baibulo Kuzikuthandizani Kwambiri

Mfundo 4 zomwe zingakuthandizeni kuti kuwerenga Baibulo kuzikuthandizani kwambiri

Kodi Ndingaphunzitse Bwanji Chikumbumtima Changa?

Chikumbumtima chanu chimasonyeza kuti ndinu munthu wotani. Chimasonyezanso mfundo zimene mumakhulupirira. Ndiye kodi chikumbumtima chanu chimasonyeza zotani zokhudza inuyo?

Kodi Ndiyenera Kubatizidwa?—Gawo 1: Tanthauzo la Kubatizidwa

Ngati mukuganiza zobatizidwa, poyamba muyenera kumvetsa tanthauzo lake.

Kodi Ndiyenera Kubatizidwa?—Gawo 2: Kukonzekera Kubatizidwa

Yankhani mafunsowa kuti muone ngati mwakonzeka kubatizidwa.

Kodi Ndiyenera Kuchita Chiyani Ndikabatizidwa?—Mbali Yoyamba: Pitirizani Kuchita Zinthu Zofunika

Pambuyo pobatizidwa, pitirizani kulimbitsa ubwenzi wanu ndi Mulungu. Pitirizani kuphunzira Baibulo, kupemphera, kuuza ena zomwe mumakhulupirira komanso kupezeka pamisonkhano yachikhristu.

Older Articles

Nkhani za M’gawo la “Zimene Achinyamata Amafunsa” M’magazini a Galamukani!

Werengani nkhani za m’gawo la “Zimene Achinyamata Amafunsa” zofalitsidwa kuyambira mu 1982 mpaka mu 2012.

Kodi Munthu Ameneyu Ndi Woyenera Kuti Ndimange Naye Banja?

Kodi n’chiyani chimene chingakuthandizeni kuti mudziwe makhalidwe enieni a mnzanuyo?

Kodi Ndithetse Chibwenzichi?—Gawo 1

Mukalowa m’banja, mukuyenera kukhala ndi mnzanuyo kwa moyo wanu wonse. Ndiye ngati mukuona kuti munthu amene muli naye pachibwenzi sangakhale woyenera kumanga naye banja, musangokhala osachitapo chilichonse.

Kodi Ndithetse Chibwenzichi?—Gawo 2

Kuthetsa chibwenzi si chinthu chophweka. Koma kodi mungatani kuti muthetse chibwenzi m’njira yabwino?